Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Amosi 3:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Bukitsani ku nyumba zacifumu za Asidodi, ndi ku nyumba zacifumu za m'dziko la Aigupto, nimuziti, Sonkhanani pa mapiri a Samariya, ndipo penyani masokosero akuru m'menemo, ndi ozunzika m'kati mwace.

Werengani mutu wathunthu Amosi 3

Onani Amosi 3:9 nkhani