Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Amosi 3:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Atero Yehova, Monga mbusa alanditsa m'kamwa mwa mkango miyendo iwiri, kapena kansonga ka khutu, momwemo adzalanditsidwa ana a Israyeli okhala pansi m'Samariya, m'ngondya ya guwa logonapo, ndi pa mitsamiro ya kama.

Werengani mutu wathunthu Amosi 3

Onani Amosi 3:12 nkhani