Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Amosi 2:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Atero Yehova, Cifukwa ca zolakwa zitatu za Moabu, kapena zinai, sindidzabweza kulanga kwace; popeza anatentha mafupa a mfumu ya ku Edomu asanduke njereza;

2. koma ndidzatumiza moto pa Moabu, udzanyeketsa nyumba zacifumu za Kerioti; ndipo Moabu adzafa ndi phokoso, ndi kupfuula, ndi mau a lipenga;

Werengani mutu wathunthu Amosi 2