Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 8:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Davide anakanthanso Hadadezeri, mwana wa Rehobu, mfumu ya ku Zoba, pomuka iye kukadzitengeranso ufumu wace ku cimtsinje ca Firate.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 8

Onani 2 Samueli 8:3 nkhani