Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 5:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo tsiku lija Davide anati, Ali yense akakantha Ajebusi, aponye m'madzi opuala ndi akhungu amene moyo wa Davide udana nao. Cifukwa cace akuti, Akhungu ndi opuala sangalowe m'nyumbamo.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 5

Onani 2 Samueli 5:8 nkhani