Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 5:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Hiramu mfumu ya Turo anatumiza mithenga kwa Davide ndi mitengo yamkungudza, ndi amisiri a matabwa, ndi omanga nyumba; iwo nammangira Davide nyumba.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 5

Onani 2 Samueli 5:11 nkhani