Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 3:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Sauli adali ndi mkazi wamng'ono, dzina lace ndiye Rizipa, mwana wa Aya. Ndipo Isiboseti anati kwa Abineri, Unalowana bwanji ndi mkazi wamng'ono wa atate wanga?

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 3

Onani 2 Samueli 3:7 nkhani