Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 24:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Davide anamangirapo Yehova guwa la nsembe, napereka nsembe zopsereza, ndi nsembe zoyamika. Momwemo Yehova anapembedzeka cifukwa ca dziko, ndi mliri wa pa Israyeli unalekeka.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 24

Onani 2 Samueli 24:25 nkhani