Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 23:29-34 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

29. Helebi mwana wa Baana Mnetofati, ltai mwana wa Ribai wa ku Gibeya wa ana a Benjamini;

30. Benaya Mpiratoni, Hidai wa ku timitsinje ta Gaasi;

31. Abialiboni M-aribati, Azmaveti Mbahurimi;

32. Eliaba Mshaliboni wa ana a Jaseni, Jonatani;

33. Sama Mharari, Ahiamu mwana wa Sarari Mharari;

34. Elifaleti mwana wa Ahasibai, mwana wa Mmaacha, Eliamu mwana wa Ahitofeli Mgiloni;

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 23