Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 23:28-39 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

28. Zalimoni M-ahohi, Maharai Mnefati;

29. Helebi mwana wa Baana Mnetofati, ltai mwana wa Ribai wa ku Gibeya wa ana a Benjamini;

30. Benaya Mpiratoni, Hidai wa ku timitsinje ta Gaasi;

31. Abialiboni M-aribati, Azmaveti Mbahurimi;

32. Eliaba Mshaliboni wa ana a Jaseni, Jonatani;

33. Sama Mharari, Ahiamu mwana wa Sarari Mharari;

34. Elifaleti mwana wa Ahasibai, mwana wa Mmaacha, Eliamu mwana wa Ahitofeli Mgiloni;

35. Hezra wa ku Karimeli, Paarai M-aribi;

36. Igali mwana wa Natani wa ku Zoba, Bani Mgadi;

37. Zeleki M-amoni, Naharai Mbeeroti, onyamula zida za Yoabu mwana wa Zeruya;

38. Ira M-itri, Garebi M-itri;

39. Uriya Mhiti; onse pamodzi anali makumi atatu mphambu asanu ndi awiri.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 23