Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 19:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ngalawa yakuolotsera inaoloka kuti akatenge banja la mfumu ndi kucita comkomera. Ndipo Simeyi mwana wa Gera anagwa pansi pamaso pa mfumu pakuoloka iye pa Yordano.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 19

Onani 2 Samueli 19:18 nkhani