Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 18:26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mlondayo anaona munthu wina wothamanga; mlonda naitana wakucipata nanena, Taona munthu wina wakuthamanga yekha. Ndipo mfumu inati, iyenso abwera ndi mau.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 18

Onani 2 Samueli 18:26 nkhani