Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 17:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Husai anatinso, Mudziwa atate wanu ndi anthu ace kuti ndizo ngwazi, ndipo ali ndi mitima yowawa monga cimbalangondo cocilanda ana ace kuthengo; ndipo atate wanu ali munthu wodziwa nkhondo, sadzagona pamodzi ndi anthu.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 17

Onani 2 Samueli 17:8 nkhani