Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 17:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Abisalomu ndi anthu onse a Israyeli anati, Uphungu wa Husai M-ariki uposa uphungu wa Ahitofeli. Pakuti kunaikidwa ndi Yehova kutsutsa uphungu wabwino wa Ahitofeli kuti Yehova akamtengere Abisalomucoipa.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 17

Onani 2 Samueli 17:14 nkhani