Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 16:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo uphungu wa Ahitofeli anaupangira masiku aja, unali monga ngati munthu anafunsira mau kwa Mulungu; uphungu wonse wa Ahitofeli unali wotere kwa Davide ndi kwa Abisalomu yemwe.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 16

Onani 2 Samueli 16:23 nkhani