Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 14:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yoabu anagwa nkhope yace pansi, namlambira, nadalitsa mfumuyo; nati Yoabu, Lero mnyamata wanu ndadziwa kuti munandikomera mtima, mbuye wanga mfumu, popeza mfumu yacita copempha mnyamata wace.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 14

Onani 2 Samueli 14:22 nkhani