Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 14:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo Yoabu mwana wa Zeruya anazindikira kuti mtima wa mfumu unalunjika kwa Abisalomu.

2. Ndipo Yoabu anatumiza ku Tekowa, natenga kumeneko mkazi wanzeru, nanena naye, Ukokomezeke monga mfedwa, nubvale zobvala za pamaliro, osadzola mafuta, koma ukhale ngati munthu wamkazi wakulira akufa nthawi yaikuru.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 14