Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 13:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunali citapita ici, popeza Abisalomu mwana wa Davide anali naye mlongo wace wokongola, dzina lace ndiye Tamara, Amnoni mwana wa Davide anamkonda iye.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 13

Onani 2 Samueli 13:1 nkhani