Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 12:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa ninji unapeputsa mau a Yehova ndi kucita cimene ciri coipa pamaso pace? Unakantha Uriya Mhiti ndi lupanga ndi kutenga mkazi wace akhale mkazi wako; ndipo unamupha iye ndi lupanga la ana a Amoni.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 12

Onani 2 Samueli 12:9 nkhani