Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 10:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ana a Amoni anaturuka, nandandalitsa nkhondo polowera kucipata. Ndipo Aaramu a ku Zoba ndi a ku Rehobu, ndi anthu a Tobu ndi Maaka, anali pa okha kuthengo.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 10

Onani 2 Samueli 10:8 nkhani