Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 9:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Wolemekezeka Yehova Mulungu wanu, wakukondwera nanu, kukuikani pa mpando wacifumu wace, mukhalire Yehova Mulungu wanu mfumu pa anthu ace; popeza Mulungu wanu anakonda Aisrayeli kuwakhazika kosatha, anakulongani mfumu yao, kucita ciweruzo ndi cilungamo.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 9

Onani 2 Mbiri 9:8 nkhani