Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 9:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo atamva mfumu yaikazi ya ku Seba mbiri ya Solomo, anadza kumuyesera Solomo ndi miyambi yododometsa ku Yerusalemu, ndi ulendo waukuru, ndi ngamila zosenza zonunkhira, ndi golidi wocuruka, ndi timiyala ta mtengo wace; ndipo atafika kwa Solomo anakamba naye zonse za m'mtima mwace.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 9

Onani 2 Mbiri 9:1 nkhani