Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 8:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anaika monga mwa ciweruzo ca Davide atate wace zigawo za ansembe ku utumiki wao, ndi Alevi ku udikiro wao, kulemekeza Mulungu, ndi kutumikira pamaso pa ansembe, monga munayenera tsiku ndi tsiku; odikira omwe monga mwa zigawo zao ku cipata ciri conse; pakuti momwemo Davide munthu wa Mulungu adamuuza.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 8

Onani 2 Mbiri 8:14 nkhani