Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 7:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mfumu Solomo anapereka nsembe ya ng'ombe zikwi makumi awiri mphambu ziwiri, ndi nkhosa zikwi, makumi awiri. Momwemo mfumu ndi anthu onse anapereka nyumba ya Yehova.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 7

Onani 2 Mbiri 7:5 nkhani