Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 6:33 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

pamenepo mumvere Inu m'Mwamba mokhala Inumo, nimumcitire mlendoyo monga mwa zonse akuitanirani; kuti mitundu yonse ya anthu a pa dziko lapansi adziwe dzina lanu, nakuopeni, monga amatero anthu anu Aisrayeli; ndi kuti adziwe kuti nyumba iyi ndamangayi ichedwa ndi dzina lanu.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 6

Onani 2 Mbiri 6:33 nkhani