Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 5:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ansembe analowa nalo likasa la cipangano la Yehova kumalo kwace m'moneneramo mwa kacisi, m'malo opatulikitsa, pansi pa mapiko a akerubi.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 5

Onani 2 Mbiri 5:7 nkhani