Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 36:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Macitidwe ena tsono a Yehoyakimu, ndi zonyansa zace anazicita, ndi zija zidapezeka zomtsutsa; taonani, zilembedwa m'buku la mafumu a Israyeli ndi Yuda; ndi Yehoyakini mwana wace anakhala mfumu m'malo mwace.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 36

Onani 2 Mbiri 36:8 nkhani