Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 35:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma Neko anatuma mithenga kwa iye, ndi kuti, Ndiri ndi ciani ndi inu, mfumu ya Yuda? sindinafika kuyambana ndi inu lero, koma ndi nyumba imene ndiri nayo nkhondo; ndipo Mulungu anati ndifulumire; lekani kubvutana ndi Mulungu amene ali nane, Iye angakuonongeni.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 35

Onani 2 Mbiri 35:21 nkhani