Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 34:17-20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

17. Nakhuthula ndarama zinapezeka m'nyumba ya Yehova, nazipereka m'manja a akapitao ndi m'manja a anchito.

18. Ndipo Safani mlembi anauza mfumu, ndi kuti, Hilikiya wansembe anandipatsa buku. Nawerengamo Safani pamaso pa mfumu.

19. Ndipo kunali, atamva mfumu mau a cilamulo, anang'amba zobvala zace.

20. Mfumu niuza Hilikiya, ndi Ahikamu mwana wa Safani, ndi Abidoni mwana wa Mikaya, ndi Safani mlembi, ndi Asaya mnyamata wa mfumu, ndi kuti,

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 34