Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 33:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pemphero lace lomwe, ndi m'mene Mulungu anapembedzeka naye, ndi chimo lace lonse, ndi kulakwa kwace, ndi apo anamanga misanje, naimika zifanizo ndi mafano osema asanadzicepetse, taonani, zalembedwa m'buku la mau a Hozai.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 33

Onani 2 Mbiri 33:19 nkhani