Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 32:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova anatuma wamthenga amene anaononga ngwazi zamphamvu zonse, ndi atsogoleri, ndi akazembe, ku cigono ca mfumu ya Asuri. Nabwerera iye ndi nkhope yamanyazi ku dziko lace. Ndipo atalowa m'nyumba ya mulungu wace, iwo oturuka m'matumbo mwace anamupha ndi lupanga pomwepo.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 32

Onani 2 Mbiri 32:21 nkhani