Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 32:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Analemberanso akalata a kunyoza Yehova Mulungu wa Israyeli, ndi kunena motsutsana ndi Iye, ndi kuti, Monga milungu ya mitundu ya anthu a m'maiko, imene siinalanditsa anthu ao m'dzanja langa, momwemo Mulungu wa Hezekiya sadzalanditsa anthu ace m'dzanja mwanga.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 32

Onani 2 Mbiri 32:17 nkhani