Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 31:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo m'nchito iri yonse anaiyamba m'utumiki wa nyumba ya Mulungu, ndi m'cilamulo, ndi m'mauzo, kufuna Mulungu wace, anacita ndi mtima wace wonse, nalemerera nayo.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 31

Onani 2 Mbiri 31:21 nkhani