Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 31:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndi Yeiyeli, ndi Azaziya, ndi Nahati, ndi Asaheli, ndi Yerimoti, ndi Yozabadi, ndi Eliyeli, ndi Ismakiya, ndi Mahati, ndi Benaya, ndiwo akapitao omvera Konaniya ndi Simei mng'ono wace, oikidwa ndi Hezekiya mfumu ndi Azariya mkuru wa ku nyumba ya Mulungu.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 31

Onani 2 Mbiri 31:13 nkhani