Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 31:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Azariya wansembe wamkuru wa nyumba ya Zadoki anamyankha, nati, Ciyambire anthu anabwera nazo zopereka ku nyumba ya Yehova, tadya, takhuta, ndipo zatitsalira zambiri; pakuti Yehova anadalitsa anthu ace; ndipo suku kucuruka kwa cotsala.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 31

Onani 2 Mbiri 31:10 nkhani