Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 30:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti mukabwera kwa Yehova, abale anu ndi ana anu adzapeza cifundo pamaso pa iwo anawatenga ndende, nadzalowanso m'dziko muno; pakuti Yehova Mulungu wanu ngwa cisomo ndi cifundo; sadzakuyang'anirani kumbali ngati mubwera kwa Iye,

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 30

Onani 2 Mbiri 30:9 nkhani