Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 30:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Hezekiya anatumiza kwa Israyeli ndi Yuda onse, nalembanso akalata kwa Efraimu ndi Manase, kuti abwere ku nyumba ya Yehova ku Yerusalemu, kucitira Yehova Mulungu wa Israyeli Paskha.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 30

Onani 2 Mbiri 30:1 nkhani