Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 29:27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nanena Hezekiya kuti apereke nsembe yopsereza pa guwa la nsembe. Ndipo pakuyamba nsembe yopsereza, inayambanso nyimbo ya Yehova ndi malipenga, pamodzi ndi zoyimbira za Davideyo mfumu ya Israyeli.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 29

Onani 2 Mbiri 29:27 nkhani