Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 25:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma ngati mumuka, citani, limbikani kunkhondo, Mulungu adzakugwetsani pamaso pa adani; pakuti Mulungu ali nayo mphamvu yakuthandiza ndi yakugwetsa.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 25

Onani 2 Mbiri 25:8 nkhani