Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 24:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mfumu inaitana Yehoyada mkuru wao, niti naye, Unalekeranji kuuza Alevi abwere nao kucokera m'Yuda ndi Yerusalemu msonkho wa Mose mtumiki wa Yehova, ndi wa msonkhano wa Israyeli, ukhale wa cihema ca umboni?

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 24

Onani 2 Mbiri 24:6 nkhani