Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 23:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma caka cacisanu ndi ciwiri Yehoyada anadzilimbitsa natenga atsogoleri a mazana, Azariya mwana wa Yeroamu, ndi Ismayeli mwana wa Yohanana, ndi Azariya mwana wa Obedi, ndi Maaseya mwana wa Adaya, ndi Elisafati mwana wa Zikiri, apangane naye pamodzi.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 23

Onani 2 Mbiri 23:1 nkhani