Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 22:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kuonongeka kwa Ahaziya tsono nkwa Mulungu, kuti amuke kwa Yehocamu; pakuti atafika anaturukira pamodzi ndi Yehoramu kukayambana ndi Yehu mwana wa Nimsi, amene Yehova anamdzoza alikhe nyumba ya Ahabu.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 22

Onani 2 Mbiri 22:7 nkhani