Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 21:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma Yehova sanafuna kuononga nyumba ya Davide cifukwa ca pangano adalicita ndi Davide, ndi monga adalonjeza kumpatsa iye ndi ana ace nyali nthawi zonse.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 21

Onani 2 Mbiri 21:7 nkhani