Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 20:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo tsopano, taonani ana a Amoni, ndi Moabu, ndi a ku phiri la Seiri, amene simunalola Israyeli awalowere, pakuturuka iwo m'dziko la Aigupto, koma anawapambukira osawaononga;

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 20

Onani 2 Mbiri 20:10 nkhani