Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 18:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mfumu ya Israyeli tsono ndi Yehosafati mfumu ya Yuda anakhala yense pa mpando wacifumu wace, obvala zobvala zacifumu zao, nakhala pamalo poyera polowera pa cipata ca Samariya; ndi aneneri onse ananenera pamaso pao.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 18

Onani 2 Mbiri 18:9 nkhani