Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 18:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo mfumu ya Israyeli anamemeza aneneri amuna mazana anai, nanena nao, Kodi timuke kunkhondo ku Ramoti Gileadi kapena ndileke? Ndipo anati, Kweraniko, pakuti Mulungu adzaupereka m'dzanja la mfumu.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 18

Onani 2 Mbiri 18:5 nkhani