Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 18:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nati Ahabu mfumu ya Israyeli kwa Yehosafati mfumu ya Yuda, Mupita nane kodi ku Ramoti Gileadi? Nayankha, nati, Monga inu momwemo ine; monga anthu anu momwemo anthu anga; tidzakhala nanu ku nkhondoyi.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 18

Onani 2 Mbiri 18:3 nkhani