Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 13:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Simunapitikitsa kodi ansembe a Yehova, ana a Aroni, ndi Alevi, ndi kudziikira ansembe monga amacita anthu a m'maiko ena? kuti ali yense wakudza kudzipatulira ndi mwana wa ng'ombe, ndi nkhosa zamphongo zisanu ndi ziwiri, yemweyo ndiye wansembe wa iyo yosati milungu.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 13

Onani 2 Mbiri 13:9 nkhani