Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 13:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anamsonkhanira amuna acabe, anthu opanda pace, ndiwo anadzilimbikitsa kutsutsana naye Rehabiamu mwana wa Solomo, muja Rehabiamu anali mnyamata ndi woolowa mtima, wosakhoza kuwalaka.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 13

Onani 2 Mbiri 13:7 nkhani