Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Mbiri 12:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Anakwera ndi magareta cikwi cimodzi mphambu mazana awiri, ndi apakavalo zikwi makumi asanu ndi limodzi, ndi anthu adadza naye kuturuka m'Aigupto ngosawerengeka, Alubi, Asuki, ndi Akusi.

Werengani mutu wathunthu 2 Mbiri 12

Onani 2 Mbiri 12:3 nkhani